Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • mwb21 September tsamba 2
  • Muzithawira ‘M’manja a Yehova Amene Adzakhalapo Mpaka Kalekale’

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Muzithawira ‘M’manja a Yehova Amene Adzakhalapo Mpaka Kalekale’
  • Kabuku ka Msonkhano wa Utumiki Komanso Moyo Wathu Wachikhristu—2021
  • Nkhani Yofanana
  • Kodi Chilamulo Chinkasonyeza Bwanji Kuti Yehova Amaganizira Akazi?
    Kabuku ka Msonkhano wa Utumiki Komanso Moyo Wathu Wachikhristu—2021
  • Kodi Chilamulo Chinkasonyeza Bwanji Kuti Yehova Amaganizira Anthu Osauka?
    Kabuku ka Msonkhano wa Utumiki Komanso Moyo Wathu Wachikhristu—2021
  • Mfundo Zothandiza Kuweruza Milandu Mwachilungamo
    Kabuku ka Msonkhano wa Utumiki Komanso Moyo Wathu Wachikhristu—2021
  • Kodi Yehova Amafuna Kuti Tizimulambira Bwanji?
    Kabuku ka Msonkhano wa Utumiki Komanso Moyo Wathu Wachikhristu—2021
Onani Zambiri
Kabuku ka Msonkhano wa Utumiki Komanso Moyo Wathu Wachikhristu—2021
mwb21 September tsamba 2
M’bale wachikulire akuwerenga Baibulo ndipo akuganizira mmene asilikali a ku Iguputo anawonongedwera m’Nyanja Yofiira.

CHUMA CHOPEZEKA M’MAWU A MULUNGU

Muzithawira ‘M’manja a Yehova Amene Adzakhalapo Mpaka Kalekale’

Yehova amafuna kuti nthawi zonse tizisonyeza makhalidwe abwino (De 33:26; it-2 51)

Yehova amatithandiza ndi mtima wonse pogwiritsa ntchito mphamvu zake (De 33:27; w11 10/15 26 ¶18)

Mofanana ndi Mose, tiyenera kukhulupirira kuti Yehova amapulumutsa anthu ake (De 33:29; w11 9/15 19 ¶16)

Manja a Yehova amene adzakhalapo mpaka kalekale amatithandiza tikamakumana ndi mayesero osiyanasiyana. Zimenezi zikuphatikizapo tikadwala kapena tikamavutika maganizo, tikaferedwa kapena tikalakwitsa zinazake n’kulapa.

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena