Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • mwb22 May tsamba 10
  • Musalole Kuti Zilakolako Zoipa Zizikulamulirani

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Musalole Kuti Zilakolako Zoipa Zizikulamulirani
  • Kabuku ka Msonkhano wa Utumiki Komanso Moyo Wathu Wachikhristu—2022
  • Nkhani Yofanana
  • Kuganizira Zoipa N’koopsa
    Utumiki Komanso Moyo Wathu wa Chikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2019
  • “Sandulikani mwa Kusintha Maganizo Anu”
    Nsanja ya Olonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzira)—2023
  • Kodi Mukukumbukira?
    Nsanja ya Olonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzira)—2019
  • Kodi Mukukumbukira?
    Nsanja ya Olonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzira)—2021
Onani Zambiri
Kabuku ka Msonkhano wa Utumiki Komanso Moyo Wathu Wachikhristu—2022
mwb22 May tsamba 10
Davide akusunzumira Batiseba kuchokera padenga la nyumba yake.

CHUMA CHOPEZEKA M’MAWU A MULUNGU

Musalole Kuti Zilakolako Zoipa Zizikulamulirani

Davide analola kuti zilakolako zoipa zikhazikike mumtima mwake (2Sa 11:2-4; w21.06 17 ¶10)

Davide anagwiritsa ntchito mphamvu zake molakwika kuti abise tchimo lomwe anachita (2Sa 11:5, 14, 15; w19.09 17 ¶15)

Davide anakumana ndi mavuto aakulu chifukwa cha tchimo lomwe anachita (2Sa 12:9-12; w18.06 17 ¶7)

Kuti tipewe kuyang’ana kapena kuganizira zinthu zolakwika, tiyenera kukhala odziletsa. (Aga 5:16, 22, 23) Yehova akhoza kutithandiza kuti zilakolako zoipa zisakhazikike mumtima mwathu.

DZIFUNSENI KUTI, ‘Kodi ndiyenera kudziletsa kwambiri ndikamaganizira zinthu ziti?

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena