Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • mwb22 May tsamba 12
  • Kudzikonda kwa Aminoni Kunabweretsa Mavuto

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Kudzikonda kwa Aminoni Kunabweretsa Mavuto
  • Kabuku ka Msonkhano wa Utumiki Komanso Moyo Wathu Wachikhristu—2022
  • Nkhani Yofanana
  • Abisalomu Anaukira Chifukwa cha Kunyada
    Kabuku ka Msonkhano wa Utumiki Komanso Moyo Wathu Wachikhristu—2022
  • Yehova ndi Mulungu Wachilungamo
    Kabuku ka Msonkhano wa Utumiki Komanso Moyo Wathu Wachikhristu—2022
  • Yehova Anachita Zinthu Mwanzeru Pogawa Malo
    Kabuku ka Msonkhano wa Utumiki Komanso Moyo Wathu Wachikhristu—2021
  • Kodi Mumapereka Nsembe?
    Kabuku ka Msonkhano wa Utumiki Komanso Moyo Wathu Wachikhristu—2022
Onani Zambiri
Kabuku ka Msonkhano wa Utumiki Komanso Moyo Wathu Wachikhristu—2022
mwb22 May tsamba 12

CHUMA CHOPEZEKA M’MAWU A MULUNGU

Kudzikonda kwa Aminoni Kunabweretsa Mavuto

Aminoni anatengeka ndi Tamara (2Sa 13:1, 2; it-1 32)

Aminoni anagwiririra Tamara (2Sa 13:10-15; w17.09 5 ¶11)

Abisalomu anachititsa kuti Aminoni aphedwe (2Sa 13:28, 29; it-1 33 ¶1)

Anthu omwe ali pa chibwenzi akucheza mosangalala ku malo odyera.

Kodi amene ali pachibwenzi angapewe bwanji mavuto? Angasonyeze kuti ndi anzeru komanso odziletsa akamapewa malo kapena zochitika zimene zingawapangitse kuti achite zolakwika.

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena