Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • mwb22 November tsamba 8
  • Kuchita Zinthu Ndi Mtima Wonse Kumabweretsa Madalitso Ambiri

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Kuchita Zinthu Ndi Mtima Wonse Kumabweretsa Madalitso Ambiri
  • Kabuku ka Msonkhano wa Utumiki Komanso Moyo Wathu Wachikhristu—2022
  • Nkhani Yofanana
  • Yoasi Anasiya Kutumikira Yehova Chifukwa Chocheza ndi Anthu Ochita Zoipa
    Nsanja ya Olonda—2009
  • Zimene Adani Athu Amachita Pofuna Kutifooketsa
    Kabuku ka Msonkhano wa Utumiki Komanso Moyo Wathu Wachikhristu—2022
  • “Tili Ndi Ambiri Kuposa Amene Ali Ndi Iwowo”
    Kabuku ka Msonkhano wa Utumiki Komanso Moyo Wathu Wachikhristu—2022
  • Mzimayi Woipa Komanso Wodzimva Analangidwa
    Kabuku ka Msonkhano wa Utumiki Komanso Moyo Wathu Wachikhristu—2022
Onani Zambiri
Kabuku ka Msonkhano wa Utumiki Komanso Moyo Wathu Wachikhristu—2022
mwb22 November tsamba 8
Elisa akupereka malangizo kwa Mfumu Yehoasi ali pabedi lake pamene akudwala. Yehoasi wanyamula mivi 4.

CHUMA CHOPEZEKA M’MAWU A MULUNGU

Kuchita Zinthu Ndi Mtima Wonse Kumabweretsa Madalitso Ambiri

Elisa anauza Mfumu Yehoasi kuti ichite zinthu zoyerekezera zosonyeza mmene Aisiraeli adzagonjetsere Asiriya (2Mf 13:15-18)

Yehoasi sanachite zinthu ndi mtima wonse ndipo zimenezi zinachititsa kuti asapambane nkhondo zonse (2Mf 13:19; w10 4/15 26 ¶11)

Yehova amadalitsa kwambiri atumiki ake amene amamufunafuna ndi mtima wonse (Ahe 11:6; w13 11/1 11 ¶5-6)

DZIFUNSENI KUTI, ‘Kodi ndimasonyeza bwanji kuti ndimachita zinthu ndi mtima wonse pa zinthu zokhudza kulambira monga kuwerenga Baibulo, kupezeka pamisonkhano komanso ntchito yolalikira?’

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena