Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • mwb23 July tsamba 4
  • Zochita za Ezara Zinachititsa Kuti Dzina la Yehova Lilemekezedwe

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Zochita za Ezara Zinachititsa Kuti Dzina la Yehova Lilemekezedwe
  • Utumiki Komanso Moyo Wathu Wachikhristu—2023
  • Nkhani Yofanana
  • Ezara Ankaphunzitsa Chilamulo cha Mulungu
    Zimene Tingaphunzire Munkhani za M’Baibulo
  • Kodi Mumaphunzitsa Zogwira Mtima?
    Nsanja ya Olonda—2002
  • Mfundo Zazikulu za M’buku la Ezara
    Nsanja ya Olonda—2006
  • Mukhoza Kukhalabe Olimba Mtima pa Nthawi Yovuta
    Nsanja ya Olonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzira)—2023
Onani Zambiri
Utumiki Komanso Moyo Wathu Wachikhristu—2023
mwb23 July tsamba 4

CHUMA CHOPEZEKA M’MAWU A MULUNGU

Zochita za Ezara Zinachititsa Kuti Dzina la Yehova Lilemekezedwe

Ezara analola kuti mawu a Mulungu azimufika pamtima ndipo zimenezi zinakhudza zochita zake (Eza 7:10; w00 10/1 14 ¶8)

Ezara anathandiza anthu ena kuzindikira nzeru za Mulungu (Eza 7:25; si 75 ¶5)

Chifukwa chakuti anadzichepetsa pamaso pa Mulungu, Ezara anali wotsimikiza mtima kuti Yehova amutsogolera komanso amuteteza (Eza 8:21-23 it-1 1158 ¶4)

Bwana akuyamikira m’bale yemwe ndi makaniko chifukwa cha ntchito imene wagwira.

Nzeru yochokera kwa Mulungu imene Ezara anasonyeza inachititsa kuti mfumu imupatse maudindo akuluakulu. Mofanana ndi Ezara, khalidwe lathu lingachititse kuti dzina la Yehova lilemekezedwe.

DZIFUNSENI KUTI, ‘Kodi anthu omwe si a Mboni amandilemekeza chifukwa chakuti ndimatsatira zimene Mulungu amafuna?’

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena