Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • mwb23 September tsamba 10
  • Moyo Ukafika Povuta

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Moyo Ukafika Povuta
  • Utumiki Komanso Moyo Wathu Wachikhristu—2023
  • Nkhani Yofanana
  • Kodi Mukukumbukira?
    Nsanja ya Olonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzira)—2020
  • Mfundo Zazikulu za M’buku la Yobu
    Nsanja ya Olonda—2006
  • Mwamuna Wachitsanzo Chabwino Amene Anavomera Kum’langiza
    Nsanja ya Olonda—2000
  • “Yembekezera Yehova”
    Nsanja ya Olonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzira)—2022
Onani Zambiri
Utumiki Komanso Moyo Wathu Wachikhristu—2023
mwb23 September tsamba 10

CHUMA CHOPEZEKA M’MAWU A MULUNGU

Moyo Ukafika Povuta

Pamene ankakumana ndi mayesero, Yobu anayerekezera moyo ndi ntchito yokakamiza (Yob 7:1; w06 3/15 14 ¶10)

Mavuto amene Yobu ankakumana nawo anam’chititsa kufotokoza momasuka mmene ankamvera (Yob 7:11)

Anafika mpaka ponena kuti akufuna kufa (Yob 7:16; w20.12 16 ¶1)

M’bale wachinyamata ali kunyumba kwa mnzake wachikulire ndipo akufotokoza nkhawa zake.

Mukaona kuti moyo wanu wafika povuta kwambiri, muzipemphera kwa Yehova mochokera pansi pamtima, kumuuza zonse zomwe zili mumtima mwanu, komanso muzifotokozera mnzanu wodalirika mmene mukumvera. Imeneyi ikhoza kukhala njira yoyamba imene ingakuthandizeni kuti muyambenso kumva bwino.—g 1/12 16-17.

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena