Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • wp21 No. 1 tsamba 16
  • Kodi Mulungu Amamva Mapemphero Anu?

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Kodi Mulungu Amamva Mapemphero Anu?
  • Nsanja ya Olonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yogawira)—2021
  • Timitu
  • Nkhani Yofanana
  • KODI BAIBULO LIMANENA ZOTANI?
  • Kodi Mulungu Amamva Mapemphero Athu?
    Nsanja ya Olonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yogawira)—2021
  • N’chifukwa Chiyani Mulungu Amafuna Kuti Tizipemphera?
    Nsanja ya Olonda Yolengeza Ufumu wa Yehova—2015
  • “Zopempha Zanu Zidziwike kwa Mulungu”
    Nsanja ya Olonda—2006
  • Tili Ndi Mwayi Wopemphera kwa Mulungu
    Zimene Baibulo Limaphunzitsa
Onani Zambiri
Nsanja ya Olonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yogawira)—2021
wp21 No. 1 tsamba 16

Kodi Mulungu Amamva Mapemphero Anu?

Mukamapemphera, kodi mumaganiza kuti Mulungu akumvadi?

KODI BAIBULO LIMANENA ZOTANI?

Mayi akuwerenga Baibulo.
  • Mulungu akumvetsera. Baibulo limanena kuti: “Yehova ali pafupi ndi onse oitanira pa iye. Iye ali pafupi ndi onse amene amamuitana m’choonadi . . . Adzamva kufuula kwawo kopempha thandizo.”​—Salimo 145:18, 19.

  • Mulungu amafuna kuti muzipemphera kwa iye. Baibulo limatiuza kuti: “Pa chilichonse, mwa pemphero ndi pembedzero, pamodzi ndi chiyamiko, zopempha zanu zidziwike kwa Mulungu.”​—Afilipi 4:6.

  • Mulungu amakuganizirani. Mulungu amadziwa nkhawa zanu zonse ndipo amafuna kukuthandizani. Baibulo limanena kuti: ‘Muzimutulira nkhawa zanu zonse, pakuti amakuderani nkhawa.’​—1 Petulo 5:7.

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena