Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • w24 July tsamba 32
  • Muziphunzira Mwakhama Kuti Mukhale Maso

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Muziphunzira Mwakhama Kuti Mukhale Maso
  • Nsanja ya Olonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzira)—2024
  • Nkhani Yofanana
  • Yehova Alonjeza Danieli Mphotho Yodabwitsa
    Samalani Ulosi wa Danieli!
  • Muziphunzira pa Chitsanzo cha Danieli
    Nsanja ya Olonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzira)—2023
  • Buku la Danieli ndi Inu
    Samalani Ulosi wa Danieli!
  • Alimbikitsidwa ndi Mthenga Wochokera kwa Mulungu
    Samalani Ulosi wa Danieli!
Onani Zambiri
Nsanja ya Olonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzira)—2024
w24 July tsamba 32

ZOTI NDIPHUNZIRE

Muziphunzira Mwakhama Kuti Mukhale Maso

Werengani Danieli 9:​1-19 kuti muone kufunika kophunzira mwakhama.

Muziona nkhani yonse. Kodi ndi zinthu ziti zomwe zinali zitangochitika kumene, nanga zinamukhudza bwanji Danieli? (Dan. 5:29–6:5) Kodi mukanakhala Danieli mukanamva bwanji?

Muzifufuza mozama. Kodi ndi “mabuku opatulika” ati omwe Danieli ankawerenga? (Dan. 9:​2, mawu a m’munsi; w11 1/1 22 ¶2) N’chifukwa chiyani iye analapa machimo ake komanso a Aisiraeli onse? (Lev. 26:​39-42; 1 Maf. 8:​46-50; dp 182-184) Kodi pemphero la Danieli likusonyeza bwanji kuti ankaphunzira Mawu a Mulungu mwakhama?—Dan. 9:​11-13.

Onani zimene mukuphunzirapo. Dzifunseni kuti:

  • ‘Kodi ndingatani kuti ndisasokonezedwe ndi zochitika za m’dzikoli?’ (Mika 7:7)

  • ‘Kodi kuphunzira Baibulo mwakhama ngati mmene Danieli ankachitira kungandithandize bwanji?’ (w04 8/1 12 ¶17)

  • ‘Kodi ndi nkhani ziti zomwe ndingaphunzire zimene zingandithandize “kukhalabe maso”?’ (Mat. 24:​42, 44; w12 8/15 5 ¶7-8)

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena