Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • ijwbq nkhani 10
  • Kodi Dzina la Mulungu Ndi Yesu?

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Kodi Dzina la Mulungu Ndi Yesu?
  • Kuyankha Mafunso a M’Baibulo
  • Timitu
  • Nkhani Yofanana
  • Yankho la m’Baibulo
  • Pankhani ya Mulungu Woona
    Nsanja ya Olonda—2008
  • Kodi Muyenera Kupemphera kwa Yesu?
    Nsanja ya Olonda—1994
  • Kodi Yesu Kristu Ndani?
    Nsanja ya Olonda—2005
  • Dzina la Mulungu
    Galamukani!—2017
Onani Zambiri
Kuyankha Mafunso a M’Baibulo
ijwbq nkhani 10
Yesu akupemphera

Kodi Dzina la Mulungu Ndi Yesu?

Yankho la m’Baibulo

Yesu ananena kuti iye ndi “Mwana wa Mulungu.” (Yohane 10:36; 11:4) Yesu sananenepo kuti iye ndi Mulungu Wamphamvuyonse.

Komanso, Yesu anapemphera kwa Mulungu. (Mateyu 26:39) Pamene ankaphunzitsa otsatira ake kupempherera, Yesu anati: “Atate wathu wakumwamba, dzina lanu liyeretsedwe.”—Mateyu 6:9.

Yesu anatchula dzina la Mulungu pamene ananena mawu ochokera m’Chilamulo kuti: “Tamverani Aisiraeli inu, Yehova Mulungu wathu ndi Yehova mmodzi.”—Maliko 12:29; Deuteronomo 6:4.

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena