-
Numeri 22:25Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
-
-
25 Buluyo ataonanso mngelo wa Yehova uja, anayamba kudzikanikizira kukhoma, moti anakanikiziranso phazi la Balamu kukhomako. Ndipo Balamu anayamba kumʼkwapulanso buluyo.
-