-
Numeri 22:25Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
-
-
25 Buluyo anaonanso mngelo wa Yehova uja. Ndipo anayamba kudzikanikizira kukhoma, moti anakanikiziranso phazi la Balamu kukhomako. Pamenepo, Balamu anayamba kum’kwapulanso kwambiri bulu uja.
-