-
Numeri 22:27Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
-
-
27 Buluyo ataonanso mngelo wa Yehova uja, anangokhala pansi, Balamu ali pamsana pake. Choncho Balamu anapsa mtima koopsa, ndipo anapitiriza kumukwapula ndi ndodo yake.
-