Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Esitere 8:9
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 9 Choncho pa nthawiyi anaitana alembi a mfumu. Limeneli linali tsiku la 23 la mwezi wachitatu womwe ndi mwezi wa Sivani.* Iwo analemba zonse zimene Moredikayi analamula Ayuda kuti achite. Makalatawo analinso opita kwa masatarapi,*+ abwanamkubwa ndi akalonga amʼzigawo zonse+ kuchokera ku Indiya mpaka ku Itiyopiya, zigawo 127. Chigawo chilichonse anachilembera mogwirizana ndi kalembedwe ka anthu akumeneko ndiponso chilankhulo chawo. Nawonso Ayuda anawalembera mogwirizana ndi kalembedwe kawo ndiponso chilankhulo chawo.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena