Miyambo 3:18 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 18 Munthu akagwiritsitsa nzeru, zidzakhala ngati mtengo wa moyo kwa iye,Ndipo anthu amene amazigwiritsitsa adzatchedwa osangalala.+ Miyambo Buku Lofufuzira Nkhani la Mboni za Yehova la 2019 3:18 Nsanja ya Olonda,5/15/1987, tsa. 28
18 Munthu akagwiritsitsa nzeru, zidzakhala ngati mtengo wa moyo kwa iye,Ndipo anthu amene amazigwiritsitsa adzatchedwa osangalala.+