-
Yesaya 23:7Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
-
-
7 Kodi uwu ndi mzinda wanu uja, umene unali wosangalala kuyambira kalekale, kuyambira pachiyambi pake?
Mapazi ake ankautengera kumayiko akutali kuti ukakhale kumeneko.
-