-
Yesaya 39:2Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
-
-
2 Hezekiya analandira anthuwo mwansangala* ndipo anawaonetsa nyumba yake yosungiramo chuma.+ Anawaonetsa siliva, golide, mafuta a basamu, mafuta ena amtengo wapatali, nyumba yake yosungiramo zida zonse zankhondo ndiponso chuma chake chonse. Palibe chimene Hezekiya sanawaonetse mʼnyumba* yake ndi mu ufumu wake wonse.
-