-
Yesaya 50:2Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
-
-
2 Ndiye nʼchifukwa chiyani nditabwera sindinapeze aliyense?
Nʼchifukwa chiyani nditaitana palibe amene anayankha?+
Kodi dzanja langa lafupika kwambiri moti silingathe kuwombola,
Kapena kodi ine ndilibe mphamvu zopulumutsira?+
Nsomba zake zimawola chifukwa chakuti mulibe madzi
Ndipo zimafa chifukwa cha ludzu.
-