-
Yeremiya 31:23Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
-
-
23 Yehova wa magulu ankhondo akumwamba, Mulungu wa Isiraeli, wanena kuti: “Ndikadzasonkhanitsa anthu a mtundu wawo amene anagwidwa nʼkutengedwa kupita kudziko lina, iwo adzanenanso mawu awa mʼdziko la Yuda ndi mʼmizinda yake kuti, ‘Yehova akudalitse iwe malo olungama okhalamo,+ iwe phiri lopatulika.’+
-