-
Ezekieli 6:9Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
-
-
9 Anthu amene adzapulumuke adzandikumbukira pakati pa anthu amitundu ina amene anawagwira ukapolo.+ Adzazindikira kuti zinandipweteka kwambiri mumtima chifukwa cha mtima wawo wosakhulupirika* womwe unachititsa kuti andipandukire+ komanso maso awo amene amalakalaka mafano awo onyansa.+ Iwo adzachita manyazi komanso kuipidwa chifukwa cha zinthu zonse zoipa ndi zonyansa zimene anachita.+
-