Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Ezekieli 31:8
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  8 Mitengo ina ya mkungudza sinafanane ndi mtengo umenewu mʼmunda wa Mulungu.+

      Panalibe mtengo uliwonse wa junipa* umene unali ndi nthambi ngati zake,

      Panalibe mtengo uliwonse wa katungulume umene nthambi zake zinali zofanana ndi za mtengowo.

      Panalibenso mtengo wina mʼmunda wa Mulungu umene unali wokongola ngati mtengo umenewu.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena