-
Ezekieli 31:8Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
-
-
8 Mitengo ina ya mkungudza sinafanane ndi mtengo umenewu mʼmunda wa Mulungu.+
Panalibe mtengo uliwonse wa junipa* umene unali ndi nthambi ngati zake,
Panalibe mtengo uliwonse wa katungulume umene nthambi zake zinali zofanana ndi za mtengowo.
Panalibenso mtengo wina mʼmunda wa Mulungu umene unali wokongola ngati mtengo umenewu.
-