Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Ezekieli 32:24
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 24 Elamu+ ali kumandako limodzi ndi gulu la anthu ake onse amene ankamutsatira ndipo anthuwo azungulira manda ake. Onsewo anaphedwa ndi lupanga. Iwo anatsikira kunthaka ali osadulidwa. Anthu amenewa anachititsa kuti anthu amene akukhala mʼdziko la anthu amoyo azikhala mwamantha. Tsopano anthu amenewa adzachita manyazi limodzi ndi anthu amene akutsikira kudzenje.*

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena