-
Ezekieli 40:23Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
-
-
23 Mʼbwalo lamkati munali geti limene linayangʼanizana ndi geti lakumpoto ndipo geti lina linayangʼanizana ndi geti lakumʼmawa. Munthu uja anayeza mtunda wochokera pageti limodzi kukafika pageti lina ndipo anapeza kuti unali mikono 100.
-