-
Ezekieli 40:34Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
-
-
34 Khonde lake linayangʼana kubwalo lakunja ndipo pazipilala zake zamʼmbali panali zithunzi za mtengo wa kanjedza ndipo anthu akafuna kulowa mʼkanyumbako amakwera masitepe 8.
-