-
Ezekieli 40:47Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
-
-
47 Kenako munthu uja anayeza bwalo lamkati. Iye anapeza kuti mulitali linali mikono 100 ndipo mulifupi linalinso mikono 100. Bwalolo linali lofanana mbali zonse 4. Guwa lansembe linali kutsogolo kwa kachisi.
-