-
Luka 11:5Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
-
-
5 Kenako anawauza kuti: “Tiyerekeze kuti mmodzi wa inu ali ndi mnzake ndipo wapita kwa mnzakeyo pakati pa usiku kukamupempha kuti, ‘Bwanawe, ndibwerekeko mitanda itatu ya mkate,
-