31 Mfumukazi yakumʼmwera+ adzaiukitsa kwa akufa pa Tsiku la Chiweruzo limodzi ndi anthu a mʼbadwo uwu ndipo idzawatsutsa, chifukwa mfumukazi imeneyi inabwera kuchokera kumalekezero a dziko lapansi kudzamva nzeru za Solomo. Koma tsopano wina woposa Solomo ali pano.+