-
Yohane 1:48Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
-
-
48 Natanayeli anamufunsa kuti: “Mwandidziwa bwanji?” Yesu anamuyankha kuti: “Filipo asanakuitane, ine ndinakuona uli pansi pa mtengo wamkuyu paja.”
-