2 ndikulembera mpingo wa Mulungu umene uli ku Korinto.+ Ndikulembera inu amene mwayeretsedwa mwa Khristu Yesu,+ amene mwaitanidwa kuti mukhale oyera, pamodzi ndi onse amene ali kulikonse omwe akuitana pa dzina la Ambuye wathu, Yesu Khristu,+ Ambuye wawo ndiponso wathu.