33 Chotero usiku umenewo iwo anakhala akupatsa vinyo bambo awo kuti azimwa.+ Kenako, mwana woyamba kubadwayo anapita n’kukagona ndi bambo akewo. Koma kuyambira pamene mwanayo anabwera kudzagona nawo mpaka pamene anachoka, bambowo sanadziwe chilichonse.