-
Ekisodo 10:19Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
-
-
19 Atatero Yehova anasintha mphepo yamphamvuyo kuti iziwomba kuchokera kumadzulo ndipo inatenga dzombelo ndi kulithira m’Nyanja Yofiira. Motero m’dera lonse la Iguputo simunatsale dzombe ngakhale limodzi.
-