-
Numeri 22:26Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
-
-
26 Tsopano mngelo wa Yehova anasunthiranso patsogolo. Anakaima pamalo ena opanikiza, pomwe panalibiretu mpata woti n’kudutsira kudzanja lamanja kapena lamanzere.
-