-
1 Mafumu 8:65Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
-
-
65 Pa nthawi imeneyo Solomo anachita chikondwerero+ pamodzi ndi Aisiraeli onse. Unali mpingo waukulu+ wa anthu amene anachokera kumadera osiyanasiyana, kuyambira polowera ku Hamati+ n’kutsetsereka mpaka kukafika kuchigwa* cha Iguputo.+ Anachita chikondwererochi pamaso pa Yehova Mulungu wathu masiku 7, ndi masiku enanso 7.+ Onse pamodzi masiku 14.
-