31 Ine ndidzaimba mlandu Yehoyakimu,+ ana ake ndi atumiki ake chifukwa cha zolakwa zawo.+ Anthu amenewa komanso anthu okhala mu Yerusalemu ndi anthu a mu Yuda ndidzawagwetsera masoka onse amene ndanena.+ Ngakhale kuti ndawauza za masoka onsewa iwo sanamvere.’”’”+