-
Yeremiya 46:16Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
-
-
16 Ambiri mwa iwo akupunthwa ndi kugwa. Ndipo akuuzana kuti: “Imirira, tiye tibwerere kwa anthu a mtundu wathu ndi kudziko la abale athu chifukwa takumana ndi lupanga loopsa.”’
-