48 Kenako ananditengera pakhonde la nyumbayo.+ Pamenepo anayeza chipilala cham’mbali cha khondelo ndipo anapeza kuti chinali mikono isanu mbali iyi ndi mikono isanu mbali inayo. M’lifupi mwa khomo la nyumbayo munali mikono itatu mbali iyi ndi mikono itatu mbali inayo.