Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Luka 8:29
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 29 (Pakuti iye anali kuuza mzimu wonyansawo kuti utuluke mwa munthuyo. Mzimu umenewu unamugwira mwamphamvu+ kwa nthawi yaitali ndithu. Mobwerezabwereza anali kumumanga ndi maunyolo komanso matangadza n’kumamuyang’anira. Koma chifukwa cha mphamvu ya chiwandacho, anali kudula maunyolowo ndi kuthawira kumalo opanda anthu.)

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena