Machitidwe 2:36 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 36 Choncho nyumba yonse ya Isiraeli idziwe ndithu, kuti Yesu ameneyu, amene inu munam’pachika,+ Mulungu anamuika kukhala Ambuye+ ndi Khristu.” Machitidwe Buku Lofufuzira Nkhani la Mboni za Yehova la 2019 2:36 Kuchitira Umboni Mokwanira, ptsa. 25-26
36 Choncho nyumba yonse ya Isiraeli idziwe ndithu, kuti Yesu ameneyu, amene inu munam’pachika,+ Mulungu anamuika kukhala Ambuye+ ndi Khristu.”