Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • sn nyimbo 34
  • Zochita Zathu Zizigwirizana ndi Dzina Lathu

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Zochita Zathu Zizigwirizana ndi Dzina Lathu
  • Imbirani Yehova
  • Nkhani Yofanana
  • Tizichita Zinthu Zogwirizana Ndi Dzina Lathu
    Imbirani Yehova Mosangalala
  • Kukhala ndi Moyo Mogwirizana ndi Dzina Lathu
    Imbirani Yehova Zitamando
  • Ntchito Yomwe Tagwira Chifukwa cha Chikondi
    Imbirani Yehova Mosangalala
  • Ntchito Imene Tagwira Chifukwa cha Chikondi
    Imbirani Yehova
Onani Zambiri
Imbirani Yehova
sn nyimbo 34

Nyimbo 34

Zochita Zathu Zizigwirizana ndi Dzina Lathu

Losindikizidwa

(Yesaya 43:10-12)

1. Yehova wamphamvu yonse wam’yaya,

Wangwiro m’chilungamo, m’chikondi.

Ndinu gwero la cho’nadi ndi nzeru,

Mulamula monga Mfumu m’mwamba.

Timakondwa pokutumikirani

Ndiponso kulengeza Ufumu.

(KOLASI)

Ndi mwayidi kukhala Mboni zanu,

Tichite monga mwa dzina lathu.

2. Pokutumikirani ndi abale

Timakhaladi mogwirizana.

Pophunzitsa ena cho’nadi chanu,

Timakhalanso osangalala.

Timadziwikanso ndi dzina lanu,

Ndi mwayi wathu kulitchukitsa.

(KOLASI)

Ndi mwayidi kukhala Mboni zanu,

Tichite monga mwa dzina lathu.

(Onaninso Deut. 32:4; Sal. 43:3; Dan. 2:20, 21.)

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena