Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • sjj nyimbo 51
  • Tadzipereka kwa Mulungu

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Tadzipereka kwa Mulungu
  • Imbirani Yehova Mosangalala
  • Nkhani Yofanana
  • Tinadzipereka kwa Mulungu!
    Imbirani Yehova
  • Tadzipatulira kwa Mulungu!
    Imbirani Yehova Zitamando
  • Moyo Wopanda Mapeto—Potsiriza!
    Imbirani Yehova Zitamando
  • Imani ndi Yehova!
    Imbirani Yehova Zitamando
Onani Zambiri
Imbirani Yehova Mosangalala
sjj nyimbo 51

NYIMBO 51

Tadzipereka kwa Mulungu

Losindikizidwa

(Mateyu 16:24)

  1. 1. M’lungu wathu watikokera kwa Khristu

    Kuti azititsogolera.

    Tadziwa choonadi

    M’lungu watiphunzitsa.

    Tikufuna kuchita

    Zofuna zake zokha.

    (KOLASI)

    Tadzipereka kwa Yehova Mulungu.

    Ndife osangalala kwambiri

  2. 2. Tamulonjeza Yehova mu pemphero

    Kuti tizimutumikira.

    Tilidi ndi chimwemwe.

    Timauzanso ena

    Za dzina la Yehova

    Ndi Ufumu wakenso.

    (KOLASI)

    Tadzipereka kwa Yehova Mulungu.

    Ndife osangalala kwambiri

(Onaninso Sal. 43:3; 107:22; Yoh. 6:44.)

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena