Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Ssb nyimbo 202
  • Tadzipatulira kwa Mulungu!

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Tadzipatulira kwa Mulungu!
  • Imbirani Yehova Zitamando
  • Nkhani Yofanana
  • Tadzipereka kwa Mulungu
    Imbirani Yehova Mosangalala
  • Tinadzipereka kwa Mulungu!
    Imbirani Yehova
  • Kristu Chitsanzo Chathu
    Imbirani Yehova Zitamando
  • Gwirizanani Nawo m’Nyimbo Yaufumu!
    Imbirani Yehova Zitamando
Onani Zambiri
Imbirani Yehova Zitamando
Ssb nyimbo 202

Nyimbo 202

Tadzipatulira kwa Mulungu!

(Eksodo 39:30)

1. Tayandikizitsidwa kwa Kristu ndi Ya.

Watitumizira cho’nadi.

Kuchoka kumwamba

Kuŵala kwafika.

Tadzikana ndipo

chidaliro chikukula.

Kwa M’lungu tadzipereka.

Tinasankha.

Tikondwa naye ndi Mwana’ke.

2. Onse odzipereka aphunzitsidwa;

Kukhala aminisitala.

Aimbadi onse

Nyimbo Yaufumu,

Mukhamu limodzi,

Popeza ndi a Mulungu.

Alumbiritsitsa mwakubatizidwa;

Nalalikira uthengawo.

3. Mwa kudzipereka kwathu tiyankhidwe

Tikhale ndi chikumbumtima.

Chimwemwe chambiri

Tichigaŵanetu

—Kusonyeza dzina.

Timfikire ndi pemphero.

Kwa M’lungu tadzipereka; tisamale

Tisunge kaimidwe kathu.

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena