Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • sjj nyimbo 142
  • Tigwire Mwamphamvu Chiyembekezo Chathu

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Tigwire Mwamphamvu Chiyembekezo Chathu
  • Imbirani Yehova Mosangalala
  • Nkhani Yofanana
  • Tigwire Mwamphamvu Chiyembekezo Chathu
    Imbirani Yehova
  • Kugwiritsitsa “Chiyembekezo Chachimwemwe”
    Imbirani Yehova Zitamando
  • Imbani Nyimbo ya Chisangalalo Chaufumu
    Imbirani Yehova Zitamando
  • Nyimbo Yatsopano
    Imbirani Yehova Mosangalala
Onani Zambiri
Imbirani Yehova Mosangalala
sjj nyimbo 142

NYIMBO 142

Tigwire Mwamphamvu Chiyembekezo Chathu

Losindikizidwa

(Aheberi 6:​18, 19)

  1. 1. Anthu akhala akuyenda mumdima

    Ndipo sizikuwathandiza n’komwe.

    Zadziwika kuti anthu ochimwa

    Sangathetse kuvutikaku.

    (KOLASI)

    Tiziimba mwachisangalalo

    Poti Ufumu wa M’lungu wayamba.

    Yesu adzachotsadi zoipa.

    Tigwire mwamphamvu chiyembekezo.

  2. 2. Uthenga womwe ukumveka ndi woti

    ‘Tsiku la Mulungu layandikira.’

    Anthu sadzakhalanso ndi chisoni.

    Tiyeni tiimbire M’lungu.

    (KOLASI)

    Tiziimba mwachisangalalo

    Poti Ufumu wa M’lungu wayamba.

    Yesu adzachotsadi zoipa.

    Tigwire mwamphamvu chiyembekezo.

(Onaninso Sal. 27:14; Mlal. 1:​14; Yow. 2:1; Hab. 1:​2, 3; Aroma 8:22.)

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena