Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • sjj nyimbo 54
  • “Njira Ndi Iyi”

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • “Njira Ndi Iyi”
  • Imbirani Yehova Mosangalala
  • Nkhani Yofanana
  • “Njira ndi Iyi”
    Imbirani Yehova
  • Moyo Wopanda Mapeto—Potsiriza!
    Imbirani Yehova Zitamando
  • Moyo Wosatha Ulonjezedwa
    Imbirani Yehova Zitamando
  • Mvetserani Mbiri ya Ufumu
    Imbirani Yehova Zitamando
Onani Zambiri
Imbirani Yehova Mosangalala
sjj nyimbo 54

NYIMBO 54

“Njira Ndi Iyi”

Losindikizidwa

(Yesaya 30:​20, 21)

  1. 1. Pali njira imene

    Munaidziwa.

    Munaphunzira za

    Njira ya mtendere

    Pamene munamvera

    Mawu a Yesu.

    Ndi njira yopezeka

    M’mawu a M’lungu.

    (KOLASI)

    Njira yakumoyo ndi yomweyi.

    Musachoke kupita kumbali.

    Mawu a Mulungu akuti

    Musachoke njira ndi yomweyi.

  2. 2. Pali njira imene

    Ndi yachikondi.

    Tikaitsatira

    Timaona kuti

    Chikondi cha Mulungu

    Ndi chochuluka.

    Nafenso tiyesetse

    Kukonda ena.

    (KOLASI)

    Njira yakumoyo ndi yomweyi.

    Musachoke kupita kumbali.

    Mawu a Mulungu akuti

    Musachoke njira ndi yomweyi.

  3. 3. Pali njira ya moyo

    Imodzi yokha.

    Palibe inanso,

    M’lungu walonjeza.

    Ndi yokhayi

    Tingapezemo chikondi.

    Njira yakumoyotu

    Ndi imeneyi.

    (KOLASI)

    Njira yakumoyo ndi yomweyi.

    Musachoke kupita kumbali.

    Mawu a Mulungu akuti

    Musachoke njira ndi yomweyi.

(Onaninso Sal. 32:8; 139:24; Miy. 6:23.)

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena