Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • sjj nyimbo 60
  • Akamvera Adzapeza Moyo

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Akamvera Adzapeza Moyo
  • Imbirani Yehova Mosangalala
  • Nkhani Yofanana
  • Akamvera Adzapeza Moyo
    Imbirani Yehova—Nyimbo Zatsopano
  • Moyo Wopanda Mapeto—Potsiriza!
    Imbirani Yehova Zitamando
  • Moyo Wosatha Ulonjezedwa
    Imbirani Yehova Zitamando
  • Khalani Omvera Kuti Mulandire Madalitso
    Imbirani Yehova
Onani Zambiri
Imbirani Yehova Mosangalala
sjj nyimbo 60

NYIMBO 60

Akamvera Adzapeza Moyo

Losindikizidwa

(Ezekieli 3:​17-​19)

  1. 1. Mulungu akufuna

    Tichenjeze anthu

    Kuti tsiku la mkwiyo

    Wake likubwera.

    (KOLASI)

    Akamvera adzapeza

    Inde moyo wosatha.

    Nafe tidzapulumuka

    Tikafalitsa uthenga,

    Uthenga.

  2. 2. Tili ndi uthenga

    Woti tiuze anthu.

    Tiitane anthu abwere

    Kwa Mulungu.

    (KOLASI)

    Akamvera adzapeza

    Inde moyo wosatha.

    Nafe tidzapulumuka

    Tikafalitsa uthenga,

    Uthenga.

    (VESI LOKOMETSERA)

    Mwamsanga tilengeze,

    Anthu amve, aphunzire.

    Adziwe choonadi

    Kuti adzapeze moyo.

    (KOLASI)

    Akamvera adzapeza

    Inde moyo wosatha.

    Nafe tidzapulumuka

    Tikafalitsa uthenga,

    Uthenga.

(Onaninso 2 Mbiri 36:15; Yes. 61:2; Ezek. 33:6; 2 Ates. 1:8.)

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena