Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • mwb16 May tsamba 5
  • Ndani Angakhale Mlendo M’chihema cha Yehova?

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Ndani Angakhale Mlendo M’chihema cha Yehova?
  • Utumiki Komanso Moyo Wathu wa Chikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2016
  • Nkhani Yofanana
  • Pitirizani Kukhala Alendo a Yehova Mpaka Kalekale
    Nsanja ya Olonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzira)—2024
  • Yehova Akutiitana Kuti Tikhale Alendo Ake
    Nsanja ya Olonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzira)—2024
  • Chenjerani ndi Miseche Yovulaza!
    Nsanja ya Olonda—1989
  • Kodi Ndani Angakhale Bwenzi la Mulungu?
    Nsanja ya Olonda—1989
Onani Zambiri
Utumiki Komanso Moyo Wathu wa Chikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2016
mwb16 May tsamba 5

CHUMA CHOPEZEKA M’MAWU A MULUNGU | MASALIMO 11-18

Ndani Angakhale Mlendo M’chihema cha Yehova?

Kuti munthu akhale mlendo m’chihema cha Yehova ayenera kukhala mnzake wa Mulungu ndipo ayenera kumukhulupirira ndi kumumvera. Salimo 15 limafotokoza zimene Yehova amafuna kuti mabwenzi ake azichita.

MLENDO WA YEHOVA AYENERA . . .

  • kukhala ndi mtima wosagawanika

  • kunena zoona, ngakhale mumtima mwake

  • kulemekeza atumiki a Yehova anzake

  • kukwaniritsa zimene walonjeza ngakhale ataona kuti n’zovuta kuchita zimenezo

  • kuthandiza anthu ovutika popanda kuyembekezera kuti amubwezere

MLENDO WA YEHOVA AMAPEWA . . .

  • miseche ndi bodza

  • kuchitira anzake zoipa

  • kudyera masuku pamutu Akhristu anzake

  • kugwirizana ndi anthu amene satumikira kapena kumvera Yehova

  • kulandira ziphuphu

Chihema
    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena