Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • mwb16 July tsamba 5
  • Anthu a Mulungu ndi Odzipereka Potumikira Yehova

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Anthu a Mulungu ndi Odzipereka Potumikira Yehova
  • Utumiki Komanso Moyo Wathu wa Chikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2016
  • Nkhani Yofanana
  • Khalani Odzipereka pa Kulambira Koona
    Nsanja ya Olonda—2010
  • ‘Zinthu Zimenezo Uziziphunzitsa kwa Anthu Okhulupirika’
    Nsanja ya Olonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzira)—2017
  • Mafunso Ochokera kwa Owerenga
    Nsanja ya Olonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzira)—2024
  • Kodi Mutsanzira Kudzipereka kwa Yehova ndi Yesu pa Nyengo ya Chikumbutso Ikubwerayi?
    Utumiki Wathu wa Ufumu—2015
Onani Zambiri
Utumiki Komanso Moyo Wathu wa Chikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2016
mwb16 July tsamba 5

CHUMA CHOPEZEKA M’MAWU A MULUNGU | MASALIMO 69-73

Anthu a Mulungu ndi Odzipereka Potumikira Yehova

Tiyenera kumachita zinthu zosonyeza kuti ndife odzipereka kwa Mulungu

69:9

  • Pa moyo wake wonse, Davide anali wodzipereka kwambiri potumikira Yehova

  • Davide sankalola kuti anthu azinyoza dzina la Yehova

Davide akupita kukakumana ndi Goliati ndi msilikali wake womunyamulira zida

Akhristu achikulire angathandize achinyamata kukhala odzipereka

Davide akuwerenga mpukutu limodzi ndi mnyamata

71:17, 18

  • Munthu amene analemba Salimo limeneli, yemwe mwina ndi Davide, ankafunitsitsa kudzalimbikitsa m’badwo wa m’tsogolo

  • Makolo komanso Akhristu odziwa zambiri, angathandize achinyamata kuti azikonda Yehova

Tikakhala odzipereka timafunitsitsa kuuza ena zimene Ufumu wa Mulungu udzatichitire

72:3, 12, 14, 16-19

  • Anthu awiri akupatsana moni

    Vesi 3​—Aliyense adzakhala pamtendere

  • Munthu wosauka akuthandizidwa

    Vesi 12​—Mulungu adzalanditsa anthu osauka

  • Mfuti ikuthyoledwathyoledwa

    Vesi 14​—Sikudzakhalanso anthu achiwawa

  • Zakudya zambiri zokwanira aliyense

    Vesi 16​—Kudzakhala chakudya cha mwana alirenji

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena