Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • mwb17 August tsamba 6
  • Gogi wa ku Magogi Awonongedwa Posachedwapa

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Gogi wa ku Magogi Awonongedwa Posachedwapa
  • Utumiki Komanso Moyo Wathu wa Chikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2017
  • Nkhani Yofanana
  • Mafunso Ochokera kwa Owerenga
    Nsanja ya Olonda Yolengeza Ufumu wa Yehova—2015
  • “Ine Ndikupatsa Chilango Iwe Gogi”
    Yehova Wabwezeretsa Kulambira Koyera
  • Imani ndi Kupenya Chipulumutso cha Yehova!
    Nsanja ya Olonda—2003
Utumiki Komanso Moyo Wathu wa Chikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2017
mwb17 August tsamba 6

CHUMA CHOPEZEKA M’MAWU A MULUNGU | EZEKIELI 35-38

Gogi wa ku Magogi Awonongedwa Posachedwapa

Baibulo limafotokoza zimene zidzachitike Gogi wa ku Magogi asanawonongedwe komanso akadzawonongedwa.

  • Babulo Wamkulu akuwonongedwa

    Chiv. 17:16-18

    Kodi chisautso chachikulu chidzayamba ndi kuwonongedwa kwa chiyani?

  • Asilikali a Gogi wa ku Magogi akukaukira atumiki a Mulungu

    Ezek. 38:2, 11, 15

    Kodi anthu a Yehova adzaukiridwa ndi ndani?

  • Dzuwa likuunikira dziko lapansi

    Chiv. 16:16

    Kodi Yehova adzawononga Gogi wa ku Magogi pankhondo iti?

  • Khristu wakhala pampando wake wachifumu kumwamba

    Chiv. 20:4

    Kodi Khristu adzalamulira kwa zaka zingati?

Kodi ndingatani kuti ndidzakhale wokonzeka pamene Gogi wa ku Magogi adzaukire anthu a Mulungu?

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena