Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • yb15 tsamba 80-tsamba 81 ndime 1
  • Dominican Republic

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Dominican Republic
  • Buku Lapachaka la Mboni za Yehova la 2015
Buku Lapachaka la Mboni za Yehova la 2015
yb15 tsamba 80-tsamba 81 ndime 1
Chithunzi chachikulu patsamba 80

Dominican Republic

MU 1492, Christopher Columbus anapita m’mayiko ena amene ankaona kuti akhoza kupezako chuma ndi zinthu zina zabwino. Pa mayikowa, panali chilumba china chimene iye anachipatsa dzina loti La Isla Española kapena kuti Hispaniola. Panopa, mbali yaikulu ya chilumbachi ili m’dziko la Dominican Republic. Masiku ano, anthu ambiri a m’dzikoli atulukira zinthu zina zofunika kwambiri. Iwo aphunzira zoti dziko latsopano likubwera ndipo mudzakhala chilungamo chifukwa lizidzalamulidwa ndi Ufumu wa Mulungu. (2 Pet. 3:13) Werengani nkhani yosangalatsa ya anthu amtima wabwino amene anaphunzira zinthu zimenezi.

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena