Zamkatimu
MUTU TSAMBA
9 1. “Ngakhale Kuti Anafa, Iye Akulankhulabe”—ABELE
17 2. “Anayenda Ndi Mulungu Woona”—NOWA
25 3. Tate wa Onse Okhala Ndi Chikhulupiriro—ABULAMU
33 4. “Kumene Inu Mupite Inenso Ndipita Komweko”—RUTE
42 5. Anali “Mkazi Wabwino Kwambiri”—RUTE
51 6. Anapemphera Kuchokera Pansi pa Mtima—HANA
59 7. “Anapitiriza Kukula, Akukondedwa Ndi Yehova”—SAMUELI
67 8. Anakhalabe Wokhulupirika Ngakhale Kuti Anakumana Ndi Mavuto—SAMUELI
76 9. Anachita Zinthu Mwanzeru—ABIGAYELI
84 10. Sanasunthike pa Kulambira Koona—ELIYA
92 11. Anali Watcheru Ndiponso Anadikira—ELIYA
99 12. Analimbikitsidwa Ndi Mulungu Wake—ELIYA
108 13. Anaphunzira pa Zolakwa Zake—YONA
116 14. Anaphunzira Kufunika Kochitira Ena Chifundo—YONA
125 15. Analimba Mtima Kuteteza Anthu a Mulungu—ESITERE
135 16. Anachita Zinthu Mwanzeru, Molimba Mtima Ndiponso Moganizira Ena—ESITERE
145 17. “Ndinetu Kapolo wa Yehova!”—MARIYA
153 18. ‘Anaganizira Tanthauzo la Mawu Onsewo Mumtima Mwake’—MARIYA
162 19. Ankasamalira Banja Lake Komanso Anakhalabe Wokhulupirika—YOSEFE
172 20. “Ndimakhulupirira”—MARITA
180 21. Anathetsa Mantha Ndiponso Mtima Wokayikira—PETULO
188 22. Anakhalabe Wokhulupirika pa Nthawi Yovuta—PETULO
196 23. Mbuye Wake Anam’phunzitsa Kufunika Kokhala Wokhululuka—PETULO
206 Mawu Omaliza