Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • mwb19 September tsamba 8
  • Kodi Mudzatani pa Nthawi ya Chilala?

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Kodi Mudzatani pa Nthawi ya Chilala?
  • Utumiki Komanso Moyo Wathu wa Chikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2019
  • Nkhani Yofanana
  • Muzikhulupirira Abale Anu
    Nsanja ya Olonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzira)—2022
  • Kukhulupirira Ena N’kofunika Kwambiri Kuti Munthu Akhale Wosangalala
    Nsanja ya Olonda—2003
  • Pangani Yehova Kukhala Chikhulupiriro Chanu
    Nsanja ya Olonda—1988
  • Muzidalira Yehova Pamene Mapeto Akuyandikira
    Nsanja ya Olonda—2011
Onani Zambiri
Utumiki Komanso Moyo Wathu wa Chikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2019
mwb19 September tsamba 8
Mtengo wodzalidwa m’mbali mwa madzi umabereka zipatso

MOYO WATHU WACHIKHRISTU

Kodi Mudzatani pa Nthawi ya Chilala?

Nthawi zonse tiyenera kukhulupirira komanso kudalira kwambiri Yehova. Mwachitsanzo, kukhulupirira Yehova kumatithandiza kumudalira kuti atiteteza komanso kutisamalira. (Sal. 23:1, 4; 78:22) Pamene tikuyandikira mapeto a dziko loipali, Satana walusa kwambiri moti akuchita chilichonse kuti atiukire. (Chiv. 12:12) Koma kodi n’chiyani chingatithandize kuti tisagonje?

ONERANI VIDIYO YAKUTI KODI MUDZATANI PA NTHAWI YA CHILALA? NDIPO KENAKO YANKHANI MAFUNSO OTSATIRAWA:

  1. Kodi tingakhale bwanji ngati “mtengo” wotchulidwa pa Yeremiya 17:8?

  2. Kodi “kutentha” kwina kungakhale chiyani?

  3. Kodi ‘mtengowu’ unakhudzidwa bwanji, nanga n’chifukwa chiyani?

  4. Kodi Satana amafuna kuwononga chiyani?

  5. Kodi tingafanane bwanji ndi munthu amene wakhala akukwera ndege kwa nthawi yaitali?

  6. N’chifukwa chiyani tiyenera kupitirizabe kudalira kapolo wokhulupirika ndi wanzeru, nanga n’chifukwa chiyani zimenezi zingakhale zovuta nthawi zina?

  7. N’chifukwa chiyani tiyenera kupitirizabe kudalira mfundo za m’Baibulo ngakhale pamene anthu ena akutinyoza?

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena