Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • mwb24 March tsamba 4
  • March 11-17

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • March 11-17
  • Utumiki Komanso Moyo Wathu wa Chikhristu—Kabuku ka Msonkhano—2024
Utumiki Komanso Moyo Wathu wa Chikhristu—Kabuku ka Msonkhano—2024
mwb24 March tsamba 4

MARCH 11-17

SALIMO 18

Nyimbo Na. 148 ndi Pemphero | Mawu Oyamba (1 min.)

CHUMA CHOPEZEKA M’MAWU A MULUNGU

1. “Yehova Ndi . . . Amene Amandipulumutsa”

(10 min.)

Yehova ali ngati thanthwe, malo achitetezo komanso chishango (Sl 18:1, 2; w09 5/1 14 ¶4-5)

Yehova amamva kulira kwathu kopempha thandizo (Sl 18:6; it-2 1161 ¶7)

Yehova amachitapo kanthu kuti atithandize (Sl 18:16, 17; w22.04 3 ¶1)

Davide akuotha moto ndipo akuganizira mmene Yehova wakhala akumuthandizira: Chithunzi 1. Akumenyana ndi chimbalangondo. 2. Wagwada pafupi ndi mkango wakufa. 3. Wanyamula lupanga ndipo waponda Goliati amene wagona pansi.

Yehova akhoza kusankha kutichotsera mayesero ngati mmene nthawi zina ankachitira ndi Davide. Komabe, nthawi zambiri Mulungu amapereka “njira yopulumukira” mwa kutipatsa zimene timafunikira kuti tithe kupirira mayeserowo.​—1Ak 10:13.

2. Mfundo Zothandiza

(10 min.)

  • Sl 18:10​—N’chifukwa chiyani yemwe analemba salimoli ananena kuti Yehova anakwera pakerubi? (it-1 432 ¶2)

  • Kodi ndi mfundo ziti zimene mwapeza pa kuwerenga Baibulo kwa mlungu uno?

3. Kuwerenga Baibulo

(4 min.) Sl 18:20-39 (th phunziro 10)

KUPHUNZITSA MWALUSO MU UTUMIKI

4. Kukoma Mtima​—Zomwe Yesu Anachita

(7 min.) Nkhani yokambirana. Onerani VIDIYO, kenako kambiranani kabuku ka lmd phunziro 3 mfundo 1-2.

5. Kukoma Mtima​—Zomwe Mungachite Potsanzira Yesu

(8 min.) Nkhani yokambirana kuchokera mu kabuku ka lmd phunziro 3 mfundo 3-5 ndi “Onaninso Malemba Awa.”

MOYO WATHU WA CHIKHRISTU

Nyimbo Na. 60

6. Zofunika Pampingo

(5 min.)

7. Vidiyo ya Zimene Gulu Lathu Lachita ya March

(10 min.) Onerani VIDIYOYI.

8. Phunziro la Baibulo la Mpingo

(30 min.) bt mutu 7 ¶1-8, bokosi patsamba 53

Mawu Omaliza (3 min.) | Nyimbo Na. 69 ndi Pemphero

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena